Malawi National Anthem Lyrics, Mlungu dalitsani Malawi,

Malawi National Anthem Lyrics,

Mlungu dalitsani Malawi,

Malawi National Song Lyrics

 

 

Mlungu dalitsani Malawi,

Mumsunge m’mtendere.

Gonjetsani adani onse,

Njala, nthenda, nsanje.

Lunzitsani mitima yathu,

Kuti tisaope.

Mdalitse Mtsogo leri na fe,

Ndi Mai Malawi.

Malawi ndziko lokongola,

La chonde ndi ufulu,

Nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,

Ndithudi tadala.

Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,

N’mphatso zaulere.

Nkhalango, madambo abwino.

Ngwokoma Malawi.

O! Ufulu tigwirizane,

Kukweza Malawi.

Ndi chikondi, khama, kumvera,

Timutumikire.

Pa nkhondo nkana pa mtendere,

Cholinga n’chimodzi.

Mai, bambo, tidzipereke,

Pokweza Malawi.

English Words

O God bless our land of Malawi,

Keep it a land of peace.

Put down each and every enemy,

Hunger, disease, envy.

Join together all our hearts as one,

That we be free from fear.

Bless our leader, each and every one,

And Mother Malawi.

Our own Malawi, this land so fair,

Fertile and brave and free.

With its lakes, refreshing mountain air,

How greatly blest are we.

Hills and valleys, soil so rich and rare,

Give us a bounty free.

Wood and forest, plains so broad and fair,

All-beauteous Malawi.

Freedom ever, let us all unite

To build up Malawi.

With our love, our zeal and loyalty,

Bringing our best to her.

In time of war, or in time of peace,

One purpose and one goal.

Men and women serving selflessly

Madagascar National Song Lyrics,

malawi national anthem english,
malawi national anthem mp3 download,
best national anthem lyrics,
morocco national anthem,
mali national anthem,
tanzania national anthem,
usa national anthem,
mauritania national anthem

Leave a Comment